Kufunafuna chipulumutso
*ziwani kuti masewera ampira ndi tchimo pamaso pa Mulungu*
Sizonse zomwe malemba adaonesa kutsusana nazo pozitchula kuti usamenye mpira ai
Komano mogilisa ntchito malemba ena timapeza tathauzo loti mpira suli oyenera kwa ana a Mulungu
Monga mau amati *chosalungama chilichonse ndi ntchimo* izitu zikutanthauza kuti ngati chinthu chomwe ukuchotacho sichikumusalasa Mulungu ndiye kuti wasangalada oipao monga ; mpira,kuvemara mau/nyimbo/sewero lasamulemekeza Mulungu
Mu BIBLE pomwe pakupezeka mau a mpira ndi Yesaya 22:18
Iye ndithu adzakuzunguza, ndi kukuponyaponya ngati mpira m'dziko lalikulu; kumeneko iwe udzafa, ndipo kumeneko kudzakhala magaleta a ulemerero wako, iwe wochititsa manyazi banja la mbuye wako.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the place of worship
Telephone
Website
Address
Machinga