Kufunafuna chipulumutso

Kufunafuna chipulumutso

Share

04/11/2025

*ziwani kuti masewera ampira ndi tchimo pamaso pa Mulungu*

Sizonse zomwe malemba adaonesa kutsusana nazo pozitchula kuti usamenye mpira ai
Komano mogilisa ntchito malemba ena timapeza tathauzo loti mpira suli oyenera kwa ana a Mulungu
Monga mau amati *chosalungama chilichonse ndi ntchimo* izitu zikutanthauza kuti ngati chinthu chomwe ukuchotacho sichikumusalasa Mulungu ndiye kuti wasangalada oipao monga ; mpira,kuvemara mau/nyimbo/sewero lasamulemekeza Mulungu

Mu BIBLE pomwe pakupezeka mau a mpira ndi Yesaya 22:18
Iye ndithu adzakuzunguza, ndi kukuponyaponya ngati mpira m'dziko lalikulu; kumeneko iwe udzafa, ndipo kumeneko kudzakhala magaleta a ulemerero wako, iwe wochititsa manyazi banja la mbuye wako.

Want your place of worship to be the top-listed Place Of Worship in Machinga?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Telephone

Website

Address


Machinga