Islamic Guide Malawi
Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh
Monga umo ndinalonjezera iyi ndi hadith yofooka tisamale
330- حديث: ((سُئل النبي صلى الله عليه وسلم عن رجل قبَّل امرأته وهما صائمان؟ قال: قد أفطرَا)).
الدرجة : لا يصح.
Anafunsidwa mtumiki saw kuti mzibambo wina anakuhaga mkazi wake swaum ili mkamwa ndipo mtumiki saw adanena kuti munthu ameneyo wsmasula swaum yake
Hadith imeneyi tisaimvere siyoona ayi
Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh!
Nthawi ija ndi iyi today or tomorrow tikhala tikulandila mulendo wabwino kwambiri Ramadhaan.
Komano m'mwezi umenewu pamene ambiri amakhala akukolola zabwino Ena akhala busy kupeza nsambi ponyoza azitsogoleri achisilamu M'malawi muno.
Mwezi uno ndipomwe timaona ma Fatwa opangidwa ndi anthu osasoma ndipo aliyense amakhala Ali ndi kukamwa kwakukuru pochilankhulira chisilamu
Abale tiyeni tizimuopa Allah
Mtumiki Muhammad saw adalankhula kuti⤵️
من أضمن لي ما بين الحييه ورجليه أضمن بي الي ابجنة
Munthu yemwe angapanilile zapakati pandevu ndi miyendo adzatetezedwa naye poikidwa ku jannah
Apa.amatanthauza yemwe angasunhe lilime ndiumaliseche
Tsopano kafukufuku wapeza kuti ngati kuli dziko limodzi lomwe anthu ake amatukwana atsogoleri awo ndi kuno kwathu Kumalawi tiyeni tilape
Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh
Nthawi zonse okondeka abale anga achisilamu tiyeni tisaiwale imfa
Mtumiki wathu Muhammad saw adatilangiza kuti,
لا تنسوا الموت فإن الموت لا ينساك
Tisaiwale imfa chifukwa imfa siimatiiwala ayi
Assalaam alykum brothers and sisters
Muli bwanji kulikonse komwe muliliko?
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Telephone
Address
Area 49
Lilongwe