Islamic Guide Malawi

Islamic Guide Malawi

Share

23/03/2024

Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh

Monga umo ndinalonjezera iyi ndi hadith yofooka tisamale

330- حديث: ((سُئل النبي صلى الله عليه وسلم عن رجل قبَّل امرأته وهما صائمان؟ قال: قد أفطرَا)).

الدرجة : لا يصح.

Anafunsidwa mtumiki saw kuti mzibambo wina anakuhaga mkazi wake swaum ili mkamwa ndipo mtumiki saw adanena kuti munthu ameneyo wsmasula swaum yake

Hadith imeneyi tisaimvere siyoona ayi

10/03/2024

Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh!

Nthawi ija ndi iyi today or tomorrow tikhala tikulandila mulendo wabwino kwambiri Ramadhaan.

Komano m'mwezi umenewu pamene ambiri amakhala akukolola zabwino Ena akhala busy kupeza nsambi ponyoza azitsogoleri achisilamu M'malawi muno.

Mwezi uno ndipomwe timaona ma Fatwa opangidwa ndi anthu osasoma ndipo aliyense amakhala Ali ndi kukamwa kwakukuru pochilankhulira chisilamu

Abale tiyeni tizimuopa Allah

Mtumiki Muhammad saw adalankhula kuti⤵️

من أضمن لي ما بين الحييه ورجليه أضمن بي الي ابجنة
Munthu yemwe angapanilile zapakati pandevu ndi miyendo adzatetezedwa naye poikidwa ku jannah

Apa.amatanthauza yemwe angasunhe lilime ndiumaliseche

Tsopano kafukufuku wapeza kuti ngati kuli dziko limodzi lomwe anthu ake amatukwana atsogoleri awo ndi kuno kwathu Kumalawi tiyeni tilape

24/10/2023

Assalaam alykum warahmatullah wabarakaatuh

Nthawi zonse okondeka abale anga achisilamu tiyeni tisaiwale imfa

Mtumiki wathu Muhammad saw adatilangiza kuti,

لا تنسوا الموت فإن الموت لا ينساك

Tisaiwale imfa chifukwa imfa siimatiiwala ayi

27/11/2022

Assalaam alykum brothers and sisters

Muli bwanji kulikonse komwe muliliko?

Want your place of worship to be the top-listed Place Of Worship in Lilongwe?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Telephone

Address


Area 49
Lilongwe