LILONGWE CCAP
CHICHEWA SERVICE
TSIKU:17 May 2026
06/05/2026
Lero Abusa DF Zembeni omwe ndi m'busa wa Lilongwe CCAP komanso Abusa ena anali limodzi ndi Mlaliki , Reine Coetzee, wochokera ku Cape Town mādziko la South Africa,yemwe ali mdziko muno paulendo wake wapadera woyenda wapansi kupita ku Israel, atanyamula mtanda ngati chizindikiro cholalikira uthenga wa chipulumutso cha Yesu Khristu.
Iye adayamba ulendowu pa 16 March chaka chatha ku South Africa, ndipo mpaka pano wakwanitsa kuyenda makilomita okwana 3,382 wapansi. Pa ulendowu wadutsa m'maiko monga Mozambique ndi Zimbabwe, ndipo pakali pano akupita ku Tanzania.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the place of worship
Telephone
Website
Address
M1 Road
Lilongwe