Prophet Y Simujah
NDI ANTHU OCHEPA KWAMBIRI OMWE AMAYAMBA CHI KRISTU NDIKUCHIMALIZA MOYENERA.
➖Ngati munthu sakukwanisa kumvera bwino-bwino Mulungu,amagwa,apo ayi amalowedwa mizimu ya chisocheretso.
➖Timayenera tikhale anthu omvera kwambiri ngakhale mu zithu zomwe sizikutipasa tanthauzo.🙌
KHALIDWE NDILOFUNIKA KWAMBIRI
🌹Ena adati Khalidwe ndi chuma,mau amenewa ndi anzeru kwambiri chifukwa ndaona anthu ambiri akulephera kupeza znthu zabwno kamba kosowa Khalidwe.
🌹Asikana ambiri akulephera kupeza ma banja abwno chifukwa chosowa Khalidwe,ena mwano,ena Kuzikuza,ena chipongwe ndipo ena chifukwa Cha moyo wawo wa social.🙌
KULIKHIDWA KWA MTENGO WAUTALI KU MALAWI 🇲🇼💔
➖Zithu Zina zooneka ngati zosakoma zikamachitika ku Dziko anthu ambiri amangoganiza kuti akuchita ndi satan.
➖Ayi ndithu,Zina zimakhala kuti akuchita ndi Mulungu kuti anthu amphunzilepo kathu {Alape}.
➖Mtengowu mu Dziko lauzimu ndimaona kuti akuulikha ndi Mulungu mwini osati Satan,ndpo Mtengowu wakhala ukupasidwa ma WARNING ochuluka koma udaumisa khosi kamba ka mapangano adziko lapansi omwe udalowa.
⚠️Mtengowu ukalikhidwa anthu ambiri ku Dziko azayakhula zosiyana-siyana zonyoza anthu ena koma omwe mungawelenge post yi musazayakhule nawo chifukwa akupanga izi ndi Mulungu mwini.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Contact the place of worship
Telephone
Address
Machinjiri Khama
Blantyre