I Cris mony intertainment

I Cris mony intertainment

Share

28/04/2026

get well soon madhala zeze ๐Ÿ’–๐Ÿ’–

18/02/2026

chabweratu oh

04/02/2026

Nyamatayu Akuti anavara uniform ya tchemwari (dress) wake chifukwa choti iyeyo alibe uniform, aphuzitsi kuwona izi anamutulutsa , ndipo apopo azake akumuwowoza.

Zikuoneka nyamatayu Ali ndi mtima wofunitsitsa school koma mavuto sakumulora kuti izi zikhale zotheka pa moyowake.

Pamene ena akutaya nsima, ena akugona ndi njala, pamene ena mukusitha zovara kanayi pa patsiku ena akuchita kuzisowa zovara zolongosoka

Dziko ndilokondera.

04/02/2026

komatu anthu inu Anthu atutumuka ndi kanema wa CCTV ku Nairobi amene akuonesa wantchito wa m'nyumba akumuyamwitsa mwana wa abwana ake mkaka wa ngati mamina koma boys zafika apa ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ

01/02/2026

ndiye kuli anthu ophunzira koma ali mbuli yotheratu mawu amodzi kwa mayi ameneyi

31/01/2026

Dzaka 47 opanda mwana๐Ÿ˜ญ๐Ÿ’”๐Ÿ’”๐Ÿ’”.

Mayi wazaka 70 zakubadwa wabeleka mwana wake oyamba dzulo.

Mayiyo akuti akhala akulira pamaso pamulungu kufuna mwana, ndipo adayitenga mimba mu 2025 mpaka dzulo wamuona mwana wankazi mmanja mwake.

Mulungu ngwabwino๐Ÿ™

31/01/2026

mupatseni ndalama yake munthuyi ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ๐Ÿคฃ

Photos from I Cris mony intertainment's post 29/01/2026

nkhani yatipeza chakumene eeeeeshy azimayi why ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญZoopsatu ๐Ÿ’”๐Ÿ’”๐Ÿ’”๐Ÿ’”Mmayi ali pa chithunziyo ndi mzika ya dziko la South Africa waombera ndi kupha Mwana wa dzaka 5 ali pachithuziyo mdela la Hammaskraal mdziko la South Africa, Nkhani ikuti mwanayu amasewela ndi anzake paja pa fupi ndi nyumba ya mayiyu,

Ndiye zikumveka Kuti mmayiyu anawauza anawa Kuti akusokosa akasewere kwina, Koma anawo anangochoka kanthawi kochepa kenaka abwereranso, basi mmayiyu kungotuluka ndi mfuti ndikumuombela mwanayu emwe anafera pomwepo,

Ndiye zikumveka Kuti mwanayu Makolo ake ndi ovutikirako basitu mmayiyu kupita Kwa Makolo ake amwanayu kuwauza Kuti mukatseketsa mulandu wu ku police ndikuthandizani chilichonse mpaka Mwana wanu aikidwe mmanda,Koma Makolo wo sanalore,

dzulo mmayiyu analowa court momwe amayankha mulandu okupha, Ndipo court litamufunsa chifukwa chomwe anapangira izi iyeyo anayankha kuti iyeyo sanaombele mwanayo dala koma amawaonetsa amzake mfuti yake ya tsopano yomwe wagula ndiye mwatsoka zinapezeka anaombera mwanayo, pakanali Pano amukana bail mlandu wake ulowanso court masiku akubwerawa๐Ÿ™„๐Ÿ™„๐Ÿ™„

Sidenote:Uyu afere kundende ndi oipa

28/01/2026

W@pha ana Ake omwe ๐Ÿ˜ข๐Ÿ’”๐Ÿ˜ญ

Ku Kenya amayi mukuwawonawo akuti atayambana ndi mamuna wake, iye basitu anaphika phala ndikutsira poyizoni ndikuwapatsa ana Ake onse atatu ndipo anawo analandira phalaro mwachikondi ndi sangala kuti amayi amatikonda atiphikira phala zachisoni anawo atadya anagoyamba kusaza magaz! Kenakoo kuphupha ndikufera pompoo amayiwo akuwona.

Zosezi akuti anachita Ati pofuna kumukhaulitsa mamuna wake ๐Ÿ˜ข๐Ÿ˜ข๐Ÿ˜ข๐Ÿ’”

Padakali Pano zimayiyu Ali maja mwa apolice

_________
Abale mukuti ndi chani ichichii ๐Ÿ˜ข๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ

27/01/2026

STEENBERG-CAPETOWN

Mammawa omwe Uno chamma 6 ,
Anthu ena amuwombela Wina wake akugona mnyumba mwake ndipo wafelatu pompo...
Izi zachitika mu Crestway.

Want your public figure to be the top-listed Public Figure in Machinga?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Category

Website

Address

Machinga