Blessed SOULS Ministries Int.

Blessed SOULS  Ministries Int.

Share

12/07/2022

Ngakhale zinthu zitafika pothina, musalore machenjera a satana kukuiwalitsani zabwino zomwe Yehova wakukonzerani. Muzikumbukira kuti satana kwakwe ndi kuba, kupha ndi kuononga. Tsono Kodi Inu mudzapindulanji kupeza DZIKO lonse nkutaya moyo (soul) wanu (Mateyu 16:26)?
Pewani tembelero lomwe Mulungu waika Kwa onse odzigulitsa okha Kwa satana, wonyengayo ( 1 Mafumu20:21).

Mzimu woyera awalitse njira yanu kuti muzindikire machenjera a mdaniyo mdzina la Yesu. Ame.

Want your place of worship to be the top-listed Place Of Worship in Lilongwe?
Click here to claim your Sponsored Listing.

Telephone

Website

Address

Nathenje
Lilongwe