NRC
13/11/2025
*TIKUFUNA KUMVA MAGANIZO ANU*
Kodi kwa inuyo, *Prosperity* kapena kuti *Kutukuka* ngati dziko mumangofokoze motani monga aMalawi.
Tikunenatu inu a Malawi omwe tinamenyeledwa ufulu kuyambila John Chilembwe, kubwela kwa Kamuzu mpaka pano tikunena kuti ndi dziko lotsata democracy.
Inuyo pa nkhani ya Prosperity kapena kuti Kutukuka ngati dziko mungakufotokezele bwanji?
n'kutani?
tili pati ngati dziko?
okhutira?
timakhumba titafika pati ngati dziko?
Timve maganizo anu!
Osaiwala kupanga follow our page.
Like and share the post.
Want your organization to be the top-listed Government Service in Lilongwe?
Click here to claim your Sponsored Listing.
Click here to claim your Sponsored Listing.
Category
Telephone
Website
Address
Lilongwe